Malaysia Native Anthem Text - Unknown


Voter pour Malaysia Native Anthem Text :
Voter Voter Voter Voter Voter Voter Voter Voter Voter Voter
Tweeter

Paroles de Unknown - Malaysia Native Anthem Text

1.

Mlungu dalitsani Malawi,

Mumsunge m'mtendere.

Gonjetsani adani onse,

Njala, nthenda, nsanje.

Lunzitsani mitima yathu,

Kuti tisaope.

Mdalitse Mtsogo leri na fe,

Ndi Mai Malawi.

2.

Malawi ndziko lokongola,

La chonde ndi ufulu,

Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,

Ndithudi tadala.

Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,

N'mphatso zaulere.

Nkhalango, madambo abwino.

Ngwokoma Malawi.

3.

O! Ufulu tigwirizane,

Kukweza Malawi.

Ndi chikondi, khama, kumvera,

Timutumikire.

Pa nkhondo nkana pa mtendere,

Cholinga n'chimodzi.

Mai, bambo, tidzipereke,

Pokweza Malawi.

Sent by Carlos Andr Pereira da Silva Branco

Imprimer Malaysia Native Anthem Text - Unknown

Video de Unknown - Malaysia Native Anthem Text

Commentaires sur Unknown - Malaysia Native Anthem Text

Aucun commentaire sur Malaysia Native Anthem Text pour l'instant...

Commenter la musique de Unknown - Malaysia Native Anthem Text

D'autres titres de Unknown

Thématique sur la chanson : Malaysia Native Anthem Text de Unknown

Haut de page